Genesis 12:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Odalitsa iwe ndidzawadalitsa, ndipo otemberera iwe ndidzawatemberera.+ Mabanja onse a padziko lapansi adzapeza madalitso* chifukwa cha iwe.”+ Numeri 23:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Pamenepo Balamu anayamba kulankhula mwa ndakatulo,+ kuti:“Balaki mfumu ya Mowabu yandiitana kuchokera ku Aramu,+Kuchokera kumapiri a kum’mawa, kuti:‘Bwera, udzanditembererere Yakobo.Bwera, udzaitanire tsoka pa Isiraeli.’+ Yoswa 24:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Kenako Balaki mwana wa Zipori,+ mfumu ya Mowabu, ananyamuka kukamenyana ndi Isiraeli.+ Iye anaitanitsa Balamu, mwana wa Beori, ndi kumuuza kuti akutemberereni.+ Nehemiya 13:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 chifukwa iwowa sanachingamire ana a Isiraeli kuti awapatse chakudya+ ndi madzi.+ M’malomwake, analemba ganyu Balamu+ kuti awatemberere.+ Koma Mulungu wathu anasintha temberero limenelo kukhala dalitso.+
3 Odalitsa iwe ndidzawadalitsa, ndipo otemberera iwe ndidzawatemberera.+ Mabanja onse a padziko lapansi adzapeza madalitso* chifukwa cha iwe.”+
7 Pamenepo Balamu anayamba kulankhula mwa ndakatulo,+ kuti:“Balaki mfumu ya Mowabu yandiitana kuchokera ku Aramu,+Kuchokera kumapiri a kum’mawa, kuti:‘Bwera, udzanditembererere Yakobo.Bwera, udzaitanire tsoka pa Isiraeli.’+
9 Kenako Balaki mwana wa Zipori,+ mfumu ya Mowabu, ananyamuka kukamenyana ndi Isiraeli.+ Iye anaitanitsa Balamu, mwana wa Beori, ndi kumuuza kuti akutemberereni.+
2 chifukwa iwowa sanachingamire ana a Isiraeli kuti awapatse chakudya+ ndi madzi.+ M’malomwake, analemba ganyu Balamu+ kuti awatemberere.+ Koma Mulungu wathu anasintha temberero limenelo kukhala dalitso.+