Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 29:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Kenako tinatenga dziko lawo ndi kulipereka monga cholowa kwa fuko la Rubeni, fuko la Gadi ndi hafu ya fuko la Manase.+

  • Yoswa 12:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Mose mtumiki wa Yehova ndi ana a Isiraeli ndiwo anagonjetsa mafumuwa.+ Atatero, Mose mtumiki wa Yehova anapereka dzikoli kwa Arubeni,+ Agadi,+ ndi hafu ya fuko la Manase,+ kuti likhale lawo.

  • Yoswa 22:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Mose anali atapatsa hafu ya fuko la Manase cholowa ku Basana.+ Hafu ina ya fukolo, Yoswa anaipatsa cholowa pamodzi ndi abale awo kutsidya lina la Yorodano kumadzulo.+ Ndipo Yoswa anawadalitsa pamene anawauza kuti azipita kumahema awo.

  • 1 Mbiri 5:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ana a Rubeni, Agadi, ndi hafu ya fuko la Manase amene anali amuna amphamvu,+ onyamula chishango ndi lupanga, odziwa kupinda uta, ndi odziwa kumenya nkhondo, analipo asilikali 44,760.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena