Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 29:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Kenako utenge mafuta odzozera+ ndi kuwathira pamutu pake ndi kum’dzoza.+

  • Ekisodo 30:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 “Koma iweyo utenge mafuta awa onunkhira, abwino koposa:+ madontho oundana a mule*+ masekeli 500, sinamoni*+ wonunkhira bwino hafu ya muyezo wa mule, kapena kuti masekeli 250, ndi kalamasi* wonunkhira+ wokwana masekeli 250.

  • Levitiko 8:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Pomalizira, Mose anathira ena mwa mafuta odzozera pamutu pa Aroni ndi kum’dzoza kuti akhale wopatulika.+

  • Salimo 133:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Zili ngati mafuta abwino amene athiridwa pamutu,+

      Amene akutsikira kundevu,

      Ndevu za Aroni,+

      Amenenso akuyenderera mpaka m’khosi la zovala zake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena