Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 91:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Pakuti adzalamula angelo ake za iwe,+

      Kuti akuteteze m’njira zako zonse.+

  • Salimo 121:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Yehova adzakuteteza ku masoka onse.+

      Iye adzateteza moyo wako.+

  • Yohane 17:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 “Komanso, ine sindikhalanso m’dzikoli pakuti ndikubwera kwa inu, koma iwo adakali m’dzikoli.+ Atate Woyera, ayang’anireni+ chifukwa cha dzina lanu limene mwandipatsa, kuti akhale amodzi mmene ife tilili.+

  • 1 Petulo 1:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 inuyo amene Mulungu akukutetezani ndi mphamvu yake chifukwa muli ndi chikhulupiriro.+ Mulungu akukutetezani kuti mudzalandire chipulumutso,+ ndipo chipulumutso chimenechi chidzaonekera+ mu nthawi ya mapeto.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena