Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 8:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Pambuyo pake, Aleviwo azitumikira pachihema chokumanako.+ Chotero uwayeretse, ndi kuwauza kuti ayende uku ndi uku monga nsembe yoweyula.+

  • 2 Mbiri 31:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Kenako Hezekiya anaika magulu+ a ansembe ndi Alevi+ mogwirizana ndi magulu awo. Gulu lililonse analiika mogwirizana ndi utumiki wawo monga ansembe+ ndi Alevi+ ogwira ntchito yokhudza nsembe yopsereza+ ndi nsembe zachiyanjano.+ Anawaika m’maguluwa kuti azitumikira,+ kuyamika+ ndi kutamanda+ Mulungu m’zipata za kachisi wa Yehova.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena