Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 13:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Pamenepo Kalebe+ anayesa kukhalitsa chete anthuwo pamaso pa Mose, kenako anati: “Tiyeni tipite tsopano lino, tikalanda dzikolo, pakuti tikaligonjetsa ndithu.”+

  • Numeri 14:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Inu simudzalowa m’dziko limene ndinachita kukweza dzanja langa+ polumbira kuti ndidzakhala nanu mmenemo, kupatula Kalebe mwana wa Yefune, ndi Yoswa mwana wa Nuni.+

  • Numeri 14:38
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 38 Koma mwa amuna amene anakazonda dzikolo, Yoswa mwana wa Nuni ndi Kalebe mwana wa Yefune, adzakhalabe ndi moyo ndithu.”’”+

  • Numeri 34:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Amunawo mayina awo ndi awa: Pa fuko la Yuda,+ Kalebe mwana wa Yefune, +

  • 1 Mbiri 4:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Ana a Kalebe+ mwana wa Yefune+ anali Iru, Ela, ndi Naamu. Mwana wa Ela anali Kenazi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena