Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 14:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Ndiyeno Mlevi,+ popeza alibe gawo kapena cholowa monga iwe, komanso mlendo wokhala pakati panu,+ mwana wamasiye* ndi mkazi wamasiye+ wokhala mumzinda wanu, azibwera kudzadya ndi kukhuta kuti Yehova Mulungu wako akudalitse+ pa chilichonse+ chimene dzanja lako likuchita.

  • Deuteronomo 15:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Mulimonse mmene zingakhalire uzim’patsa zimene akufunazo,+ ndipo mtima wako usakhale woumira pomupatsa zinthu zimenezo, chifukwa ukakhala wowolowa manja, Yehova Mulungu wako adzakudalitsa pa chilichonse chimene ukuchita ndi pa ntchito zako zonse.+

  • Salimo 67:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Mulungu adzatidalitsa,+

      Ndipo malekezero onse a dziko lapansi adzamuopa.+

  • Salimo 115:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Yehova adzadalitsa anthu omuopa,+

      Adzadalitsa onsewo osasiyapo aliyense.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena