Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 147:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Amauza Yakobo mawu ake,+

      Ndipo amauza Isiraeli malangizo+ ake ndi zigamulo zake.+

  • Miyambo 2:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 ukamazifunafuna ngati siliva,+ ndi kuzifufuza ngati chuma chobisika,+

  • Yesaya 45:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Ine sindinalankhule m’malo obisika,+ m’malo amdima a padziko lapansi. Sindinauze mbewu ya Yakobo kuti, ‘Anthu inu muzindifunafuna pachabe.’+ Ine ndine Yehova, wolankhula zolungama, wonena zowongoka.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena