Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 20:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Ndipo Mulungu anayamba kulankhula mawu awa, kuti:+

  • Deuteronomo 33:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Iye analinso kukonda anthu ake.+

      Oyera awo onse ali m’manja mwanu.+

      Iwowa anakhala pansi, pamapazi panu.+

      Anayamba kulandira ena mwa mawu anu.+

  • Salimo 78:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Mulungu anaika chikumbutso pakati pa ana a Yakobo,+

      Iye anaika chilamulo mu Isiraeli,+

      Zinthu zimene analamula makolo athu,+

      Kuti auze ana awo.+

  • Salimo 103:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Anauza Mose njira zake,+

      Ndipo anadziwitsa ana a Isiraeli zochita zake.+

  • Aroma 9:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Amenewa ndi Aisiraeli,+ amene Mulungu anawatenga kukhala ana ake.+ Anawapatsanso ulemerero,+ mapangano,+ Chilamulo,+ utumiki wopatulika+ ndi malonjezo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena