Ekisodo 20:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 20 Ndipo Mulungu anayamba kulankhula mawu awa, kuti:+ Deuteronomo 33:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Iye analinso kukonda anthu ake.+Oyera awo onse ali m’manja mwanu.+Iwowa anakhala pansi, pamapazi panu.+Anayamba kulandira ena mwa mawu anu.+ Salimo 78:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Mulungu anaika chikumbutso pakati pa ana a Yakobo,+Iye anaika chilamulo mu Isiraeli,+Zinthu zimene analamula makolo athu,+Kuti auze ana awo.+ Salimo 103:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Anauza Mose njira zake,+Ndipo anadziwitsa ana a Isiraeli zochita zake.+ Aroma 9:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Amenewa ndi Aisiraeli,+ amene Mulungu anawatenga kukhala ana ake.+ Anawapatsanso ulemerero,+ mapangano,+ Chilamulo,+ utumiki wopatulika+ ndi malonjezo.+
3 Iye analinso kukonda anthu ake.+Oyera awo onse ali m’manja mwanu.+Iwowa anakhala pansi, pamapazi panu.+Anayamba kulandira ena mwa mawu anu.+
5 Mulungu anaika chikumbutso pakati pa ana a Yakobo,+Iye anaika chilamulo mu Isiraeli,+Zinthu zimene analamula makolo athu,+Kuti auze ana awo.+ Salimo 103:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Anauza Mose njira zake,+Ndipo anadziwitsa ana a Isiraeli zochita zake.+ Aroma 9:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Amenewa ndi Aisiraeli,+ amene Mulungu anawatenga kukhala ana ake.+ Anawapatsanso ulemerero,+ mapangano,+ Chilamulo,+ utumiki wopatulika+ ndi malonjezo.+
4 Amenewa ndi Aisiraeli,+ amene Mulungu anawatenga kukhala ana ake.+ Anawapatsanso ulemerero,+ mapangano,+ Chilamulo,+ utumiki wopatulika+ ndi malonjezo.+