Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 26:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Pamapeto pake Yehova anatitulutsa mu Iguputo ndi dzanja lamphamvu+ ndi mkono wotambasula,+ zoopsa zazikulu,+ zizindikiro ndi zozizwitsa.+

  • Salimo 78:49
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 49 Anawasonyeza mkwiyo wake woyaka moto,+

      Ukali, ziweruzo zamphamvu ndi masautso.+

      Anawatumizira makamu a angelo obweretsa masoka.+

  • Yeremiya 32:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Inu munatulutsa anthu anu Aisiraeli m’dziko la Iguputo+ pogwiritsa ntchito zizindikiro, zozizwitsa,+ dzanja lamphamvu, mkono wotambasula ndi zinthu zochititsa mantha kwambiri.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena