Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 22:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 n’kumuuza kuti: “Yehova wati, ‘Ndikulumbira+ pali dzina langa, kuti chifukwa cha zimene wachitazi, posakana kupereka mwana wako yekhayo,+

  • Ekisodo 32:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Kumbukirani Abulahamu, Isaki ndi Isiraeli atumiki anu, amene munawalumbirira pa inu mwini,+ powauza kuti, ‘Ndidzachulukitsa mbewu yanu ngati nyenyezi zakumwamba,+ ndipo dziko lonseli limene ndalipatula ndidzalipereka kwa mbewu yanu,+ kuti likhale lawo mpaka kalekale.’”+

  • Deuteronomo 10:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Koma Yehova anadziphatika kwa makolo anu ndi kuwakonda, moti anasankha ana awo obadwa m’mbuyo mwawo,+ inuyo, pakati pa anthu onse monga mmene zilili lero.

  • Salimo 105:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Wakumbukira pangano limene anapangana ndi Abulahamu,+

      Ndi lonjezo limene analumbira kwa Isaki,+

  • Luka 1:73
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 73 lumbiro limene analumbira kwa kholo lathu lakale Abulahamu,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena