Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 7:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Yehova Mulungu wako adzawapereka ndithu kwa iwe ndipo udzawagonjetse.+ Udzawawononge ndithu+ ndipo usadzachite nawo pangano kapena kuwakomera mtima.+

  • Deuteronomo 20:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Mizinda yokhayi ya anthu awa a mitundu ina imene Yehova Mulungu wanu akukupatsani monga cholowa, ndi imene simuyenera kusiyamo chilichonse chopuma chili chamoyo,+

  • Yoswa 10:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Yoswa analanda mzinda wa Makeda+ tsiku limenelo ndipo anapha anthu a mumzindawo ndi lupanga. Mfumu ya mzindawo ndi anthu ake onse anawapha,+ ndipo Yoswa anaonetsetsa kuti pasakhale wopulumuka. Mfumu ya ku Makeda+ anaichita zofanana ndi zomwe anachita mfumu ya ku Yeriko.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena