Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 27:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Mukawoloka Yorodano+ ndi kulowa m’dziko limene Yehova Mulungu wanu akukupatsani, muimike miyala ikuluikulu ndi kuipaka utoto woyera.

  • Yoswa 4:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Chotero ana a Isiraeliwo anachita monga mmene Yoswa anawalamulira. Anapita pakati pa mtsinje wa Yorodano, ndipo anakanyamula miyala 12 mogwirizana ndi chiwerengero cha mafuko a ana a Isiraeli,+ monga mmene Yehova analamulira Yoswa. Ananyamula miyalayo ndi kukaiika kumalo awo ogona.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena