Salimo 74:16 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 16 Usana ndi wanu, usikunso ndi wanu.+Inu munapanga chounikira, munapanga dzuwa.+ Salimo 135:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Chilichonse chimene Yehova anafuna kuchita anachita.+Anachita zimenezi kumwamba, padziko lapansi, m’nyanja ndi m’madzi onse akuya.+ Salimo 136:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Amenenso anapanga dzuwa kuti lizilamulira masana:+Pakuti kukoma mtima kwake kosatha kudzakhalapobe mpaka kalekale.+ Mateyu 19:26 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 26 Yesu anawayang’anitsitsa n’kunena kuti: “Kwa anthu zimenezi n’zosathekadi, koma zinthu zonse n’zotheka kwa Mulungu.”+
6 Chilichonse chimene Yehova anafuna kuchita anachita.+Anachita zimenezi kumwamba, padziko lapansi, m’nyanja ndi m’madzi onse akuya.+
8 Amenenso anapanga dzuwa kuti lizilamulira masana:+Pakuti kukoma mtima kwake kosatha kudzakhalapobe mpaka kalekale.+ Mateyu 19:26 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 26 Yesu anawayang’anitsitsa n’kunena kuti: “Kwa anthu zimenezi n’zosathekadi, koma zinthu zonse n’zotheka kwa Mulungu.”+
26 Yesu anawayang’anitsitsa n’kunena kuti: “Kwa anthu zimenezi n’zosathekadi, koma zinthu zonse n’zotheka kwa Mulungu.”+