Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 74:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Usana ndi wanu, usikunso ndi wanu.+

      Inu munapanga chounikira, munapanga dzuwa.+

  • Salimo 135:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Chilichonse chimene Yehova anafuna kuchita anachita.+

      Anachita zimenezi kumwamba, padziko lapansi, m’nyanja ndi m’madzi onse akuya.+

  • Salimo 136:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Amenenso anapanga dzuwa kuti lizilamulira masana:+

      Pakuti kukoma mtima kwake kosatha kudzakhalapobe mpaka kalekale.+

  • Mateyu 19:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Yesu anawayang’anitsitsa n’kunena kuti: “Kwa anthu zimenezi n’zosathekadi, koma zinthu zonse n’zotheka kwa Mulungu.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena