Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 10:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Yehova anaperekanso mzindawo ndi mfumu yake m’manja mwa Isiraeli. Choncho Aisiraeli anapha anthu onse a mumzindawo ndi lupanga, ndipo anaonetsetsa kuti pasakhale wopulumuka. Mfumu ya ku Libina anaichita zofanana ndi zomwe anachita mfumu ya ku Yeriko.+

  • Yoswa 10:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Yehova anapereka Lakisi m’manja mwa Isiraeli, moti analanda mzindawo pa tsiku lachiwiri. Anapha ndi lupanga munthu aliyense amene anali mumzindawo,+ mofanana ndi zonse zimene anachita ku Libina.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena