Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 2:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Kuchokera ku Aroweli,+ mzinda umene uli m’mbali mwa chigwa cha Arinoni, ndiponso kuchokera kumzinda wa m’chigwa mpaka ku Giliyadi, panalibe mzinda womwe unali wa malinga aatali kwambiri kwa ife.+ Yehova Mulungu wathu anawapereka onsewo kwa ife.

  • Oweruza 11:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Pamene Aisiraeli anali kukhala ku Hesiboni ndi m’midzi yake yozungulira,+ ku Aroweli+ ndi m’midzi yake yozungulira ndi m’mizinda yonse ya m’gombe la Arinoni kwa zaka 300, n’chifukwa chiyani simunawalande mizindayo pa nthawi imeneyo?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena