Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 49:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 “Chakudya chochokera kwa Aseri chidzakhala chonona,+ ndipo chakudya chokoma cha mfumu chidzachokera kwa iye.+

  • Deuteronomo 33:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Kwa Aseri anati:+

      “Aseri ndi wodalitsidwa ndi ana aamuna.+

      Akhale wovomerezeka ndi abale ake,+

      Woponda phazi lake m’mafuta.+

  • Luka 2:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Kunalinso Anna mneneri wamkazi, mwana wa Fanueli, wa fuko la Aseri. Mayi ameneyu anali wachikulire kwambiri, ndipo anakhala ndi mwamuna wake zaka 7 zokha kuchokera pa unamwali wake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena