Ekisodo 6:25 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 25 Ndipo Eleazara mwana wa Aroni,+ anatenga mwana wamkazi wa Putieli kukhala mkazi wake. Ndipo iye anam’berekera Pinihasi.+ Amenewa ndiwo atsogoleri a mabanja a m’fuko la Levi, malinga ndi mzere wobadwira wa makolo awo.+ Numeri 25:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Koma Pinihasi+ mwana wa Eleazara, mdzukulu wa wansembe Aroni, ataona zimenezi nthawi yomweyo ananyamuka pakati pa khamulo n’kutenga mkondo waung’ono m’dzanja lake. Yoswa 22:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Kenako ana a Isiraeli anatumiza+ Pinihasi+ mwana wa wansembe Eleazara, kwa ana a Rubeni, ana a Gadi, ndi hafu ya fuko la Manase, ku Giliyadi. Yoswa 24:33 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 33 Nayenso Eleazara mwana wa Aroni anamwalira.+ Choncho anamuika m’manda m’phiri la Pinihasi mwana wake,+ limene anapatsidwa m’dera lamapiri la Efuraimu. Salimo 106:30 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 30 Pinihasi ataimirira ndi kuchitapo kanthu,+Mliriwo unatha.
25 Ndipo Eleazara mwana wa Aroni,+ anatenga mwana wamkazi wa Putieli kukhala mkazi wake. Ndipo iye anam’berekera Pinihasi.+ Amenewa ndiwo atsogoleri a mabanja a m’fuko la Levi, malinga ndi mzere wobadwira wa makolo awo.+
7 Koma Pinihasi+ mwana wa Eleazara, mdzukulu wa wansembe Aroni, ataona zimenezi nthawi yomweyo ananyamuka pakati pa khamulo n’kutenga mkondo waung’ono m’dzanja lake.
13 Kenako ana a Isiraeli anatumiza+ Pinihasi+ mwana wa wansembe Eleazara, kwa ana a Rubeni, ana a Gadi, ndi hafu ya fuko la Manase, ku Giliyadi.
33 Nayenso Eleazara mwana wa Aroni anamwalira.+ Choncho anamuika m’manda m’phiri la Pinihasi mwana wake,+ limene anapatsidwa m’dera lamapiri la Efuraimu.