Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 2:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Yehova akawapatsa oweruza,+ Yehova anali kukhaladi ndi aliyense wa oweruzawo, ndipo iye anali kuwapulumutsa m’manja mwa adani awo masiku onse a moyo wa woweruzayo. Yehova anali kuchita zimenezo pakuti anali kuwamvera chisoni+ akamva kubuula kwawo chifukwa cha owapondereza ndi owakankhakankha.+

  • Salimo 86:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Pa tsiku la nsautso yanga ndidzaitana pa inu,+

      Ndipo inu mudzandiyankha.+

  • Salimo 107:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Iwo anayamba kuitana Yehova kuti awathandize m’masautso awo.+

      Ndipo iye anawapulumutsa ku mavuto awo monga mwa nthawi zonse.+

  • Hoseya 5:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Kenako ndidzabwerera kumalo anga kufikira iwo atalangidwa chifukwa cha zolakwa zawo+ ndipo adzayamba kufunafuna nkhope yanga.+ Zinthu zikadzawavuta,+ adzandifuna.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena