Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 7:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Yehova Mulungu wako adzawaperekadi kwa iwe ndi kuwabalalitsa atasokonezeka kwambiri, kufikira atawonongedwa.+

  • Salimo 44:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Pakuti iwo sanatenge dzikolo chifukwa cha lupanga lawo,+

      Ndipo si mkono wawo umene unawabweretsera chipulumutso.+

      Koma chinabwera ndi dzanja lanu lamanja,+ mkono wanu ndi kuwala kwa nkhope yanu,

      Chifukwa munakondwera nawo.+

  • Miyambo 3:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Uzim’kumbukira m’njira zako zonse,+ ndipo iye adzawongola njira zako.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena