Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 12:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ndiyeno amuna a ku Efuraimu anasonkhana pamodzi n’kuwolokera tsidya lina chakumpoto, ndi kuuza Yefita kuti: “N’chifukwa chiyani unawoloka kukamenya ndi ana a Amoni ife osatiitana kuti tipite nawe?+ Tikutentha ndi moto pamodzi ndi nyumba yako.”+

  • Oweruza 15:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Zitatero, Afilisiti anayamba kufunsa kuti: “Wachita zimenezi ndani?” Ndiyeno iwo anati: “Ndi Samisoni, mkamwini wa munthu wa ku Timuna uja, chifukwa chakuti anatenga mkazi wake ndi kum’pereka kwa mwamuna amene anali mnzake wa mkwati.”+ Choncho Afilisiti anapita kukatentha ndi moto mtsikanayo pamodzi ndi bambo ake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena