-
Oweruza 16:5Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
5 Pamenepo olamulira ogwirizana+ a Afilisiti anafika kwa mkaziyo ndi kumuuza kuti: “Umunyengerere+ kuti udziwe chinsinsi cha mphamvu zake zazikuluzo ndi zimene tingachite kuti timugonjetse. Ufufuzenso zimene tingam’mange nazo kuti tithane naye. Ukatero aliyense wa ife adzakupatsa ndalama zasiliva zokwana 1,100.”+
-