Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 17:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Yoswa atamva, anawayankha kuti: “Ngati muli ochuluka, kwerani mtunda mupite kunkhalango ya Aperezi+ ndi ya Arefai,+ mukaduleko mitengo n’kutenga deralo, chifukwa dera lamapiri+ la Efuraimu lakucheperani.”

  • Oweruza 10:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Pambuyo pa Abimeleki, panabwera Tola, munthu wa fuko la Isakara, amene anapulumutsa+ Isiraeli. Iye anali kukhala ku Samiri m’dera lamapiri la Efuraimu,+ ndipo anali mwana wa Puwa, amene anali mwana wa Dodo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena