Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 115:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Amene amawapanga adzafanana nawo.+

      Onse amene amawakhulupirira adzakhala ngati mafanowo.+

  • Salimo 135:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Amene amawapanga adzafanana nawo,+

      Onse amene amawakhulupirira adzakhala ngati mafanowo.+

  • Yesaya 44:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Koma mtengo wotsalawo wapangira mulungu, wapangira chifaniziro chake chosema. Wachiweramira ndi kuchigwadira n’kumapemphera pamaso pake kuti: “Ndipulumutseni, pakuti ndinu mulungu wanga.”+

  • Yeremiya 51:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Munthu aliyense wachita zinthu mopanda nzeru kwambiri moti ndi zoonekeratu kuti sakudziwa kalikonse.+ Mmisiri aliyense wa zitsulo adzachita manyazi chifukwa cha chifaniziro chake chosula.+ Pakuti chifaniziro chake chopangidwa ndi chitsulo chosungunula ndi mulungu wonama+ ndipo mafano amenewa alibe moyo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena