-
1 Samueli 11:5Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
5 Ndiyeno Sauli anatulukira kuchokera kutchire, akuyenda pambuyo pa ziweto. Kenako anati: “Kodi chachitika n’chiyani kuti anthuwa azilira?” Motero anayamba kum’fotokozera mawu a amuna a ku Yabesi.
-