Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 15:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Akisa ali pabulu pa ulendo wopita kunyumba, anakakamiza Otiniyeli kuti apemphe malo kwa Kalebe bambo ake. Ndiyeno Akisa anawomba m’manja kuitana bambo ake, ndipo Kalebe atamva, anam’funsa kuti: “Ukufuna chiyani?”+

  • 2 Mafumu 4:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Ndiyeno mayiyo anakwera bulu wake wamkazi+ n’kuuza wantchito wake kuti: “Kwera bulu utsogole. Uzithamanga, usayende pang’onopang’ono chifukwa cha ine, pokhapokha ndikakuuza.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena