Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 24:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Lero mwadzionera nokha kuti Yehova anakuperekani m’manja mwanga m’phangamu. Winawake anandiuza kuti ndikupheni,+ koma ndinakumverani chisoni n’kunena kuti, ‘Sindingatambasule dzanja langa ndi kuukira mbuyanga, pakuti iye ndi wodzozedwa+ wa Yehova.’

  • 1 Samueli 26:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Kwa ine, n’zosatheka!+ Sindingachite zimenezi pamaso pa Yehova.+ Sindingatambasule dzanja langa+ ndi kukantha wodzozedwa wa Yehova.+ Choncho, tiye titenge mkondo umene uli chakumutu kwakewo, ndi mtsuko wa madziwo tizipita.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena