Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 27:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Akisi anakhulupirira+ Davide, ndipo mumtima mwake anati: “Mosakayikira, Davide wakhala fungo lonunkha kwa anthu akwawo Aisiraeli,+ ndipo iye akhala mtumiki wanga mpaka kalekale.”

  • 1 Samueli 29:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Ndiyeno akalonga a Afilisiti anayamba kunena kuti: “Kodi Aheberi+ awa akufuna chiyani kuno?” Pamenepo Akisi anayankha akalonga a Afilisitiwo kuti: “Kodi uyu si Davide, mtumiki wa Sauli, mfumu ya Isiraeli? Iyetu wakhala ndi ine kuno kwa chaka chimodzi kapena ziwiri,+ ndipo kuyambira tsiku limene anathawira kwa ine kufikira lero, sindinam’peze+ ndi chifukwa ngakhale chimodzi.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena