Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 25:42
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 42 Kenako Abigayeli+ ananyamuka mofulumira ndi kukwera pabulu,+ atsikana ake asanu antchito akumutsatira pambuyo. Iye anatsatira nthumwi za Davide ndipo anakakhala mkazi wake.

  • 1 Samueli 27:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Davide anapitiriza kukhala ndi Akisi ku Gati. Iye anakhala kumeneko pamodzi ndi amuna amene anali kuyenda naye, ndipo aliyense mwa amunawo anali ndi banja lake.+ Davide anali ndi akazi ake awiri aja, Ahinowamu+ wa ku Yezereeli ndi Abigayeli+ wa ku Karimeli, amene anali mkazi wa Nabala.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena