Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 33:56
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 56 Zikadzatero, zimene ndinafuna kuchita kwa anthuwo ndidzachita kwa inu.’”+

  • Deuteronomo 28:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Anthu amene sunawadziwe adzadya zipatso za m’dziko lako ndi mbewu zako zonse.+ Motero udzakhala wodyeredwa ndi woponderezedwa nthawi zonse.+

  • 1 Mbiri 10:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Amuna onse a Isiraeli amene anali m’chigwa ataona kuti asilikaliwo athawa, komanso kuti Sauli ndi ana ake afa, anayamba kuchoka m’mizinda yawo ndi kuthawa.+ Kenako Afilisiti anabwera n’kuyamba kukhala m’mizindayo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena