Numeri 14:44 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 44 Komabe, anthuwo ananyamuka mwa iwo okha ulendo wopita kudera lamapiri kuja,+ koma likasa la pangano la Yehova silinachoke pakati pa msasa. Mose nayenso sanachoke.+ Yoswa 6:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Ansembe 7 aziyenda patsogolo pa Likasa atanyamula malipenga 7 a nyanga za nkhosa zamphongo. Pa tsiku la 7 mudzagube kuzungulira mzindawo maulendo 7, ansembewo akuliza malipenga.+ 1 Samueli 14:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 Pamenepo Sauli anauza Ahiya+ kuti: “Bweretsa likasa la Mulungu woona!”+ (Pakuti masiku amenewo likasa la Mulungu woona linali ndi ana a Isiraeli.)+ 2 Samueli 15:25 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 25 Ndiyeno mfumu inauza Zadoki kuti: “Tenga likasa+ la Mulungu woona ndi kubwerera nalo mumzinda.+ Yehova akandikomera mtima adzandibwezeretsa mumzinda ndipo ndidzaliona. Ndidzaonanso malo amene limakhala.+
44 Komabe, anthuwo ananyamuka mwa iwo okha ulendo wopita kudera lamapiri kuja,+ koma likasa la pangano la Yehova silinachoke pakati pa msasa. Mose nayenso sanachoke.+
4 Ansembe 7 aziyenda patsogolo pa Likasa atanyamula malipenga 7 a nyanga za nkhosa zamphongo. Pa tsiku la 7 mudzagube kuzungulira mzindawo maulendo 7, ansembewo akuliza malipenga.+
18 Pamenepo Sauli anauza Ahiya+ kuti: “Bweretsa likasa la Mulungu woona!”+ (Pakuti masiku amenewo likasa la Mulungu woona linali ndi ana a Isiraeli.)+
25 Ndiyeno mfumu inauza Zadoki kuti: “Tenga likasa+ la Mulungu woona ndi kubwerera nalo mumzinda.+ Yehova akandikomera mtima adzandibwezeretsa mumzinda ndipo ndidzaliona. Ndidzaonanso malo amene limakhala.+