Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 4:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Ndiyeno anthuwo atabwerera kumsasa, akulu a Isiraeli anayamba kunena kuti: “N’chifukwa chiyani lero Yehova watigonjetsa pamaso pa Afilisiti?+ Tiyeni tikatenge likasa la pangano la Yehova+ ku Silo, kuti likhale pakati pathu ndi kutipulumutsa m’manja mwa adani athu.”

  • 1 Samueli 5:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Kumeneko anatenga likasa la Mulungu woona ndi kulilowetsa m’nyumba ya Dagoni, n’kuliika pafupi ndi fano la Dagonilo.+

  • 1 Samueli 7:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Chotero amuna a ku Kiriyati-yearimu+ anabweradi ndi kutenga likasa la Yehova n’kupita nalo kwawo, ndipo analiika m’nyumba ya Abinadabu+ imene inali paphiri. Anapatula Eleazara mwana wake kuti azilondera likasa la Yehova.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena