Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 1:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 “‘Ngati akupereka nkhosa+ kapena mbuzi kuti ikhale nsembe yake yopsereza, azipereka+ mwana wamphongo wopanda chilema.+

  • Oweruza 6:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Ndipo umangire Yehova Mulungu wako guwa lansembe mwa kuyala miyala. Ulimange pamwamba pa linga la malo otetezekawa. Ukatero, utenge ng’ombe yaing’ono yamphongo yachiwiri ija, ndi kuipereka monga nsembe yotentha ndi moto pankhuni za mzati wopatulika umene udulewo.”

  • 1 Mafumu 18:38
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 38 Atatero, moto+ wa Yehova unatsika n’kunyeketsa nsembe yopsereza+ ija, nkhuni, miyala ndi fumbi lomwe. Unaumitsanso madzi amene anali m’ngalande muja.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena