-
1 Samueli 9:24Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
24 Pamenepo wophikayo anatenga mwendo wonse n’kuuika patsogolo pa Sauli. Atatero anati: “Nyama imene inasungidwa ija ndi imeneyi. Tenga, udye chifukwa anasungira iweyo kuti udzaidye pa nthawi ino pamodzi ndi oitanidwa.” Chotero Sauli anadya pamodzi ndi Samueli pa tsikulo.
-