Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 6:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Ndiyeno Gidiyoni analowa m’nyumba ndi kuphika nyama ya mwana wa mbuzi.+ Anatenganso ufa wokwana muyezo umodzi wa efa* ndi kupanga mikate yopanda chofufumitsa.+ Atatero, anatenga nyamayo ndi kuiika m’dengu, ndipo msuzi anauika mumphika. Kenako, anatenga zinthu zimenezi ndi kukamupatsa mngelo uja pansi pa mtengo waukulu uja.

  • Oweruza 15:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Ndiyeno patapita nthawi, m’masiku okolola tirigu, Samisoni anapita kukaona mkazi wake uja, atatenga kamwana ka mbuzi.+ Pamenepo iye anati: “Ndilowa m’chipinda cha mkazi wanga.”+ Koma bambo a mkaziyo sanam’lole kuti alowe.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena