Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 2:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Mngelo wa Yehova atalankhula mawu amenewa kwa ana onse a Isiraeli, anthuwo anayamba kulira mokweza mawu.+

  • Oweruza 21:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Ndiyeno anthuwo anapita ku Beteli+ ndi kukhala pansi kumeneko pamaso pa Mulungu woona+ mpaka madzulo. Iwo anali kulira kwambiri mofuula.+

  • 1 Samueli 30:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Pamenepo Davide ndi anthu amene anali naye anayamba kulira mofuula+ mpaka kulefuka osathanso kulira.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena