Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 20:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ndipo ana a Isiraeli ananyamuka ndi kupita ku Beteli kukafunsira kwa Mulungu,+ kuti: “Ndani wa ife ayenera kutitsogolera kunkhondo yomenyana ndi ana a Benjamini?”+ Poyankha, Yehova anati: “Yuda akutsogolereni.”+

  • Oweruza 20:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Zitatero, ana onse a Isiraeli,+ anthu onse, anapita mpaka anakafika ku Beteli. Kumeneko analira+ ndipo anakhala pansi pamaso pa Yehova ndi kusala kudya+ tsiku limenelo mpaka madzulo. Iwo anapereka nsembe zopsereza+ ndi nsembe zachiyanjano+ kwa Yehova.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena