Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 13:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Ndiyeno Sauli anadzisankhira amuna 3,000 a mu Isiraeli. Amuna 2,000 anali ndi Sauliyo ku Mikimasi+ ndi kudera lamapiri la Beteli. Amuna 1,000 anali ndi Yonatani+ ku Gibeya+ wa ku Benjamini, ndipo anthu ena onse otsalawo anawabweza kumahema awo.

  • 1 Samueli 14:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Thanthwe limodzi looneka ngati dzinolo linali kumpoto ndipo linaima ngati chipilala moyang’ana ku Mikimasi,+ ndipo linalo linali kum’mwera moyang’ana ku Geba.+

  • Yesaya 10:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Iye waukira Ayati.+ Wadutsa ku Migironi. Waika katundu wake ku Mikimasi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena