Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 74:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Kumbukirani izi: Inu Yehova, mdani wakuchitirani mopanda ulemu,+

      Ndipo anthu opusa anyoza dzina lanu.+

  • Salimo 74:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Nyamukani inu Mulungu, weruzani mlandu wanu.+

      Kumbukirani mmene munthu wopusa wakunyozerani tsiku lonse.+

  • Salimo 79:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Bwezerani anthu oyandikana nafe mwa kuwatsanulira chitonzo pachifuwa pawo maulendo 7,+

      Inu Yehova, muwabwezere chitonzo chimene anachita pa inu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena