Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 37:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Usapse mtima ndipo pewa kukwiya.+

      Usapse mtima kuti ungachite choipa.+

  • Miyambo 14:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Munthu amene amakwiya msanga amachita zinthu zopusa,+ koma munthu wotha kuganiza bwino amadedwa.+

  • Miyambo 14:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Wosafulumira kukwiya n’ngozindikira zinthu kwambiri,+ koma wokwiya msanga amalimbikitsa uchitsiru.+

  • Miyambo 27:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Mkwiyo umasefukira ndipo ukali ndi wankhanza,+ koma nsanje ndani angaipirire?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena