Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mlaliki 8:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Ineyo ndinatamanda kusangalala,+ chifukwa palibe chabwino chimene anthu angachite padziko lapansi pano kuposa kudya, kumwa ndi kusangalala, pamene akugwira ntchito mwakhama masiku onse a moyo wawo,+ amene Mulungu woona wawapatsa padziko lapansi pano.+

  • Mlaliki 12:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Komanso uzidzaopa chimene chili pamwamba ndipo m’njira mudzakhala zoopsa. Mtengo wa amondi udzachita maluwa,+ chiwala chizidzayenda mochita kudzikoka ndipo zakudya sizidzakoma,* popeza munthu adzakhala akupita kunyumba yake yokhalitsa+ ndipo olira azidzazungulira mumsewu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena