Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 17:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ndikapitiriza kudikira, ku Manda kukhala kunyumba kwanga.+

      Ndidzayala bedi langa mu mdima.+

  • Yobu 30:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Pakuti ndikudziwa bwino kuti mudzandibwezera ku imfa,+

      Kunyumba yosonkhanako aliyense wamoyo.

  • Salimo 49:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Awatsogolera ku Manda ngati nkhosa zopita kokaphedwa.+

      Imfa idzakhala m’busa wawo.+

      Ndipo m’mawa anthu owongoka mtima adzawalamulira.+

      Matupi awo adzawonongeka.+

      Aliyense wa iwo malo ake okhala ndi ku Manda, osati malo okwezeka.+

  • Mlaliki 9:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Chilichonse chimene dzanja lako lapeza kuti lichite, uchichite ndi mphamvu zako zonse,+ pakuti kulibe kugwira ntchito, kuganiza zochita, kudziwa zinthu,+ kapena nzeru,+ ku Manda*+ kumene ukupitako.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena