Ekisodo 19:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Tsopano ngati mudzalabadiradi+ mawu anga ndi kusunga pangano langa,+ pamenepo mudzakhaladi chuma changa chapadera pakati pa anthu ena onse,+ chifukwa dziko lonse lapansi ndi langa.+ Deuteronomo 32:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Pakuti gawo la Yehova ndilo anthu ake.+Yakobo ndiye gawo la cholowa chake.+ 2 Samueli 21:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Ndiyeno Davide anafunsa Agibeoni kuti: “Ndikuchitireni chiyani ndipo ndipereke chiyani kuti ndiphimbe tchimo+ limeneli, kuti inu mudalitse cholowa+ cha Yehova?”
5 Tsopano ngati mudzalabadiradi+ mawu anga ndi kusunga pangano langa,+ pamenepo mudzakhaladi chuma changa chapadera pakati pa anthu ena onse,+ chifukwa dziko lonse lapansi ndi langa.+
3 Ndiyeno Davide anafunsa Agibeoni kuti: “Ndikuchitireni chiyani ndipo ndipereke chiyani kuti ndiphimbe tchimo+ limeneli, kuti inu mudalitse cholowa+ cha Yehova?”