Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mbiri 11:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Sibekai+ Mhusati, Ilai Muahohi,+

  • 1 Mbiri 20:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ndiyeno nkhondo imeneyi itatha, panabukanso nkhondo ina ndi Afilisiti+ ku Gezeri.+ Pa nthawi imeneyo Sibekai+ Mhusati anapha Sipa, amene anali mmodzi mwa mbadwa za Arefai,+ moti Afilisiti anagonjetsedwa.

  • 1 Mbiri 27:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Mtsogoleri wa 8, wa mwezi wa 8, anali Sibekai+ Mhusati, wochokera mwa Azera.+ Gulu lake linali ndi anthu 24,000.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena