Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 44:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Ndiye chonde mbuyanga, tengani ineyo ndikhale kapolo wanu m’malo mwa mwanayu, kuti iye apite ndi abale akewa.+

  • 1 Mbiri 21:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Kenako Davide anauza Mulungu woona kuti: “Kodi si ine amene ndinalamula kuti awerenge anthu? Ndipo kodi si ine ndachimwa ndi kuchitadi cholakwa?+ Nanga nkhosazi+ zalakwa chiyani? Chonde Yehova Mulungu wanga, dzanja lanu likhale pa ine ndi panyumba ya bambo anga, koma mliriwu usakhale pa anthu anu.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena