Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 12:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Tsopano sonkhanitsani anthu otsalawo kuti muuthire nkhondo mzindawu ndi kuulanda, kuti ndisaulande ndine, kuopera kuti lingatchuke ndi dzina langa.”

  • 1 Mafumu 2:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Kenako Davide anagona limodzi ndi makolo ake,+ ndipo anaikidwa m’manda mu Mzinda wa Davide.+

  • Nehemiya 12:37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 37 Oimbawo atafika pa Chipata cha Kukasupe,+ gulu lowatsatira lija lili pambuyo pawo, anayenda pamalo okwera a mpandawo kudutsa pa Masitepe+ ochokera ku Mzinda wa Davide+ mpaka kukafika kumtunda kwa Nyumba ya Davide. Kenako anafika ku Chipata cha Kumadzi,+ kum’mawa kwa chipatacho.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena