Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 12:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Iye anayankha kuti: “Pamene mwana anali ndi moyo ndinali kusala kudya+ ndipo ndinali kulira+ chifukwa mumtima mwanga ndinali kunena kuti, ‘Angadziwe ndani, mwina Yehova angandikomere mtima ndipo mwanayu angakhale ndi moyo?’+

  • Yona 3:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Ndani angadziwe? Mwina Mulungu woona satigwetsera tsoka ndipo asintha maganizo+ ndi kubweza mkwiyo wake woyaka moto, moti satiwononga.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena