Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 15:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Taona, iwo ali ndi ana amuna awiri, Ahimazi+ mwana wa Zadoki ndi Yonatani+ mwana wa Abiyatara. Choncho amuna inu mukatume amenewa kuti adzandiuze zonse zimene mungamve.”

  • 2 Samueli 17:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Ndipo tsopano tumizani uthenga mwamsanga kwa Davide+ wakuti, ‘Lero musagone m’chipululu, muwoloke ndithu+ kuopera kuti inu mfumu pamodzi ndi anthu onse amene muli nawo mungamezedwe.’”+

  • 2 Samueli 17:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Ndiyeno atumiki a Abisalomu atachoka, Ahimazi ndi Yonatani anatuluka m’chitsimemo ndi kupita kukauza Mfumu Davide kuti: “Anthu inu nyamukani mwamsanga muwoloke mtsinje, pakuti Ahitofeli wapereka malangizo+ ndipo wanena zakutizakuti kuti athane nanu.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena