Yeremiya 40:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Ine ndikhala ku Mizipa+ kuno kuti ndizikuimirani kwa Akasidi amene adzabwera kwa ife. Koma inu, sonkhanitsani vinyo,+ zipatso za m’chilimwe* ndi mafuta ndi kuziika m’ziwiya zanu ndipo muzikhala m’mizinda imene mwaitenga kukhala yanu.” Amosi 8:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, anandionetsa masomphenya awa: Ndinaona dengu la zipatso za m’chilimwe.*+ Mika 7:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Tsoka kwa ine,+ chifukwa ndakhala ngati munthu wanjala amene sanapeze zipatso kuti adye.+ Ndakhala ngati munthu amene sanapeze nkhuyu zoyambirira zimene anali kuzilakalaka, nthawi yokolola zipatso za m’chilimwe* ndi mphesa itatha.+
10 Ine ndikhala ku Mizipa+ kuno kuti ndizikuimirani kwa Akasidi amene adzabwera kwa ife. Koma inu, sonkhanitsani vinyo,+ zipatso za m’chilimwe* ndi mafuta ndi kuziika m’ziwiya zanu ndipo muzikhala m’mizinda imene mwaitenga kukhala yanu.”
8 Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, anandionetsa masomphenya awa: Ndinaona dengu la zipatso za m’chilimwe.*+
7 Tsoka kwa ine,+ chifukwa ndakhala ngati munthu wanjala amene sanapeze zipatso kuti adye.+ Ndakhala ngati munthu amene sanapeze nkhuyu zoyambirira zimene anali kuzilakalaka, nthawi yokolola zipatso za m’chilimwe* ndi mphesa itatha.+