Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 24:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Kodi mfumu ya Isiraeli ikulondola ndani? Kodi mukuthamangitsa ndani? Zoona mukuthamangitsa galu wakufa?+ Nthata imodzi?+

  • 2 Samueli 3:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Abineri atamva mawu amenewa a Isi-boseti anakwiya kwambiri+ n’kunena kuti: “Kodi ine ndine galu+ wopanda pake wa Yuda? Ineyo ndikusonyeza kukoma mtima kosatha ku nyumba ya Sauli bambo ako, abale ake ndi mabwenzi ake apamtima, ndipo ndikukuteteza kuti usagwe m’manja mwa Davide, koma lero ukundiimba mlandu wa cholakwa chokhudza mkazi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena